Mateyu 15:17 - Buku Lopatulika17 Simudziwa kodi kuti zonse zakulowa m'kamwa zipita m'mimba, ndipo zitayidwa kuthengo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Simudziwa kodi kuti zonse zakulowa m'kamwa zipita m'mimba, ndipo zitayidwa kuthengo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Kodi inu simuzindikira kuti zonse zoloŵa m'kamwa mwa munthu zimaloŵa m'mimba mwake, pambuyo pake nkukatayidwa kuthengo? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Kodi inu simudziwa kuti chilichonse cholowa mʼkamwa chimapita mʼmimba ndipo kenaka chimatuluka kunja kwa thupi? Onani mutuwo |