Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 15:17 - Buku Lopatulika

17 Simudziwa kodi kuti zonse zakulowa m'kamwa zipita m'mimba, ndipo zitayidwa kuthengo?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Simudziwa kodi kuti zonse zakulowa m'kamwa zipita m'mimba, ndipo zitayidwa kuthengo?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Kodi inu simuzindikira kuti zonse zoloŵa m'kamwa mwa munthu zimaloŵa m'mimba mwake, pambuyo pake nkukatayidwa kuthengo?

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Kodi inu simudziwa kuti chilichonse cholowa mʼkamwa chimapita mʼmimba ndipo kenaka chimatuluka kunja kwa thupi?

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 15:17
9 Mawu Ofanana  

Nagamula fano la Baala, nagamula nyumba ya Baala, naiyesa dzala mpaka lero lino.


Ndipo Iye anati, Kodi inunso mukhala chipulukirire?


Koma zakutuluka m'kamwa zichokera mumtima; ndizo ziipitsa munthu.


chifukwa sikalowa mumtima mwake, koma m'mimba mwake, ndipo katulukira kuthengo? Ndipo potero anayeretsa zakudya zonse.


Munthu wabwino atulutsa zabwino m'chuma chokoma cha mtima wake; ndi munthu woipa atulutsa zoipa m'choipa chake: pakuti m'kamwa mwake mungolankhula mwa kuchuluka kwa mtima wake.


Zakudya ndizo za mimba, ndi mimba ndiyo ya zakudya; koma Mulungu adzathera iyi ndi izi. Koma thupi silili la chigololo, koma la Ambuye, ndi Ambuye wa thupi;


Ndipo lilime ndilo moto; ngati dziko la chosalungama mwa ziwalo zathu laikika lilime, ndili lodetsa thupi lonse, niliyatsa mayendedwe a chibadwidwe, ndipo liyatsidwa ndi Gehena.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa