Mateyu 15:14 - Buku Lopatulika14 Kawalekeni iwo, ali atsogoleri akhungu. Ndipo ngati wakhungu amtsogolera wakhungu, onse awiri adzagwa m'mbuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Kawalekeni iwo, ali atsogoleri akhungu. Ndipo ngati wakhungu amtsogolera wakhungu, onse awiri adzagwa m'mbuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Alekeni, ndi atsogoleri akhungu ameneŵa. Tsono ngati wakhungu atsogolera wakhungu mnzake, onse aŵiri adzagwa m'dzenje.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Alekeni, ndi atsogoleri osaona. Ngati munthu wosaona atsogolera wosaona mnzake, onse awiri adzagwera mʼdzenje.” Onani mutuwo |