Mateyu 15:13 - Buku Lopatulika13 Koma Iye anayankha nati, Mmera wonse, umene Atate wanga wa Kumwamba sanaubzale, udzazulidwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Koma Iye anayankha nati, Mmera wonse, umene Atate wanga wa Kumwamba sanaubzale, udzazulidwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Yesu adati, “Chomera chilichonse chimene sichidabzalidwe ndi Atate anga akumwamba, chidzazulidwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Iye anayankha kuti, “Mbewu iliyonse imene Atate anga akumwamba sanadzale idzazulidwa ndi mizu yomwe. Onani mutuwo |