Mateyu 15:11 - Buku Lopatulika11 si chimene chilowa m'kamwa mwake chiipitsa munthu; koma chimene chituluka m'kamwa mwake, ndicho chiipitsa munthu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 si chimene chilowa m'kamwa mwake chiipitsa munthu; koma chimene chituluka m'kamwa mwake, ndicho chiipitsa munthu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Si chinthu choloŵa m'kamwa mwa munthu chimene chimamuipitsa ai, koma chotuluka m'kamwa mwake ndiye chimene chimamuipitsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Chimene chimalowa mʼkamwa mwa munthu sichimuchititsa kukhala woyipa, koma chimene chimatuluka mʼkamwa mwake, icho ndi chimene chimamuchititsa kukhala woyipa.” Onani mutuwo |