Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 14:32 - Buku Lopatulika

32 Ndipo pamene iwo analowa m'ngalawamo, mphepo inaleka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 Ndipo pamene iwo analowa m'ngalawamo, mphepo inaleka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Pambuyo pake aŵiriwo adaloŵa m'chombo muja, mphepo nkuleka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Ndipo atalowa mʼbwato mphepo inaleka.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 14:32
6 Mawu Ofanana  

Ndipo pomwepo Yesu anatansa dzanja lake, namgwira iye, nanena naye, Iwe wokhulupirira pang'ono, wakayikiranji mtima?


Ndipo iwo amene anali m'ngalawamo anamgwadira, nanena, Zoonadi, ndinu Mwana wa Mulungu.


Ndipo iwo anachita mantha aakulu, nanenana wina ndi mnzake, Uyu ndani nanga, kuti ingakhale mphepo ndi nyanja zimvera Iye?


Ndipo Iye anakwera, nalowa kwa iwo m'ngalawa, ndipo mphepo inaleka; ndipo anadabwa kwakukulu mwa iwo okha;


Pamenepo analola kumlandira m'ngalawa; ndipo pomwepo ngalawayo inafika kumtunda kumene analikunkako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa