Mateyu 14:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo pomwepo Yesu anatansa dzanja lake, namgwira iye, nanena naye, Iwe wokhulupirira pang'ono, wakayikiranji mtima? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo pomwepo Yesu anatansa dzanja lake, namgwira iye, nanena naye, Iwe wokhulupirira pang'ono, wakayikiranji mtima? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Pompo Yesu adatambalitsa dzanja nkumugwira nati, “Iwe wa chikhulupiriro chochepawe, unakayikiranji?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Ndipo mofulumira Yesu anatambasula dzanja lake namugwira iye, nati, “Iwe wachikhulupiriro chochepa, bwanji unakayika?” Onani mutuwo |