Mateyu 14:33 - Buku Lopatulika33 Ndipo iwo amene anali m'ngalawamo anamgwadira, nanena, Zoonadi, ndinu Mwana wa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Ndipo iwo amene anali m'ngalawamo anamgwadira, nanena, Zoonadi, ndinu Mwana wa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Apo amene anali m'chombo aja adamgwadira Yesu nati, “Ndithudi, ndinu Mwana wa Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Pamenepo amene anali mʼbwato anamulambira Iye, nati, “Zoonadi, Inu ndinu Mwana wa Mulungu.” Onani mutuwo |