Mateyu 14:30 - Buku Lopatulika30 Koma m'mene iye anaiona mphepo, anaopa; ndipo poyamba kumira, anafuula, nati, Ambuye, ndipulumutseni ine! Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Koma m'mene iye anaiona mphepo, anaopa; ndipo poyamba kumira, anafuula, nati, Ambuye, ndipulumutseni ine! Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Koma ataona m'mene ikuwombera mphepo, adachita mantha, nkuyamba kumira. Tsono adafuula kuti, “Ambuye, pulumutseni!” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Koma ataona mphepo, iye anachita mantha ndipo anayamba kumira, nafuwula nati, “Ambuye ndipulumutseni!” Onani mutuwo |