Mateyu 14:29 - Buku Lopatulika29 Ndipo Iye anati, Idza. Ndipo Petro anatsika m'ngalawa, nayenda pamadzi, kufika kwa Yesu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Ndipo Iye anati, Idza. Ndipo Petro anatsika m'ngalawa, nayenda pamadzi, kufika kwa Yesu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Yesu adati, “Chabwino, bwera.” Tsono Petro adatuluka m'chombo nayamba kuyenda pa madzi kupita kwa Yesu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Iye anati, “Bwera.” Pamenepo Petro anatuluka mʼbwato ndipo anayenda pa madzi kupita kwa Yesu. Onani mutuwo |