Mateyu 14:26 - Buku Lopatulika26 Koma m'mene ophunzirawo anamuona Iye, alikuyenda pamadzi, ananthunthumira, nati, Ndi mzukwa! Ndipo anafuula ndi mantha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Koma m'mene ophunzirawo anamuona Iye, alikuyenda pamadzi, ananthunthumira, nati, Ndi mzukwa! Ndipo anafuula ndi mantha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Pamene ophunzira aja adamuwona akuyenda pa madzi, adaopsedwa nati, “Ndi mzukwa!” Ndipo adayamba kukuwa chifukwa cha mantha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Ophunzira atamuona akuyenda pa nyanja, anaopa nati, “Ndi mzukwa!” Ndipo analira chifukwa cha mantha. Onani mutuwo |