Mateyu 14:25 - Buku Lopatulika25 Ndipo pa ulonda wachinai wa usiku, Iye anadza kwa iwo, nayenda pamwamba pa nyanja. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndipo pa ulonda wachinai wa usiku, Iye anadza kwa iwo, nayenda pamwamba pa nyanja. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 M'mamaŵa kukali mbuu, Yesu adadza kwa iwo Iye akuyenda pa madzi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Pa ora lachinayi usiku, Yesu anabwera kwa iwo akuyendabe pa nyanja. Onani mutuwo |