Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 14:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo pa ulonda wachinai wa usiku, Iye anadza kwa iwo, nayenda pamwamba pa nyanja.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo pa ulonda wachinai wa usiku, Iye anadza kwa iwo, nayenda pamwamba pa nyanja.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 M'mamaŵa kukali mbuu, Yesu adadza kwa iwo Iye akuyenda pa madzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Pa ora lachinayi usiku, Yesu anabwera kwa iwo akuyendabe pa nyanja.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 14:25
11 Mawu Ofanana  

Woyala thambo yekha, naponda pa mafunde a panyanja.


Amene alumikiza mitanda ya zipinda zake m'madzi; naika makongwa akhale agaleta ake; nayenda pa mapiko a mphepo.


Koma dziwani ichi, kuti mwini nyumba akadadziwa nthawi yiti mbala ikudza, iye akadadikira, ndipo sakadalola kuti nyumba yake ibooledwe.


Chifukwa chake dikirani; pakuti simudziwa inu nthawi yake yakubwera mwini nyumba, kapena madzulo, kapena pakati pausiku, kapena pakulira tambala, kapena mamawa;


Ndipo pakuwaona ali kuvutidwa ndi kupalasa, pakuti mphepo inadza nikomana nao, pa ulonda wachinai wa usiku Iye anadza kwa iwo, alikuyenda pamwamba pa nyanja; nati awapitirire;


Ndipo akadza ulonda wachiwiri, kapena wachitatu, nakawapeza atero, odala amenewa.


Ndipo pamene adapalasa monga mastadiya makumi awiri ndi asanu kapena makumi atatu, anaona Yesu alikuyenda panyanja, ndi kuyandikira ngalawa; ndipo anachita mantha.


ndipo anali nako m'dzanja lake kabuku kofunyulula: ndipo anaponda nalo phazi lake lamanja panyanja, ndi lamanzerelo pamtunda,


Ndipo mngelo amene ndinamuona alikuimirira panyanja ndi pa mtunda, anakweza dzanja lake lamanja kuloza kumwamba,


Ndipo mau ndinawamva ochokera Kumwamba, analankhulanso nane, nanena, Muka, tenga buku lofunyululalo m'dzanja la mngelo wakuimirira panyanja ndi padziko.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa