Mateyu 14:20 - Buku Lopatulika20 Ndipo anadya onse, nakhuta; ndipo anatola makombo otsala, nadzala madengu khumi ndi iwiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Ndipo anadya onse, nakhuta; ndipo anatola makombo otsala, nadzala madengu khumi ndi iwiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Anthu onsewo adadya mpaka kukhuta. Pambuyo pake ophunzira aja adatola zotsala nkudzaza madengu khumi ndi aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Onse anadya nakhuta ndipo ophunzira anatola zotsalira ndi kudzaza madengu khumi ndi awiri. Onani mutuwo |