Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 14:18 - Buku Lopatulika

18 Ndipo Iye anati, Mudze nazo kuno kwa Ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ndipo Iye anati, Mudze nazo kuno kwa Ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Yesu adati, “Bwera nazoni kuno.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Koma Iye anati, “Bweretsani kwa Ine.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 14:18
4 Mawu Ofanana  

Koma iwo ananena kwa Iye, Ife tilibe kanthu pano koma mikate isanu, ndi nsomba ziwiri.


Ndipo Iye analamulira makamu a anthu akhale pansi paudzu; ndipo Iye anatenga mikate isanuyo ndi nsomba ziwirizo, ndipo m'mene anayang'ana kumwamba, anadalitsa, nanyema, napatsa mikateyo kwa ophunzira, ndi ophunzira kwa makamuwo.


Ndipo analamulira anthu a khamulo akhale pansi; natenga mikate isanu ndi iwiriyo, nayamika, nanyema, napatsa ophunzira ake, kuti apereke kwa iwo; ndipo anapereka kwa khamulo.


Nati Yesu, Akhalitseni anthu pansi. Ndipo panali udzu wambiri pamalopo. Pamenepo amunawo anakhala pansi, kuwerenga kwao monga zikwi zisanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa