Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 14:17 - Buku Lopatulika

17 Koma iwo ananena kwa Iye, Ife tilibe kanthu pano koma mikate isanu, ndi nsomba ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Koma iwo ananena kwa Iye, Ife tilibe kanthu pano koma mikate isanu, ndi nsomba ziwiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Iwo adati, “Pano tili ndi buledi msanu yekha ndi nsomba ziŵiri, basi.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Iwo anayankha kuti, “Tili ndi malofu asanu okha a buledi ndi nsomba ziwiri.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 14:17
10 Mawu Ofanana  

Koma Yesu anati kwa iwo, Iwo alibe chifukwa cha kumukira, apatseni ndinu adye.


Ndipo Iye anati, Mudze nazo kuno kwa Ine.


Kodi chikhalire simudziwa, ndipo simukumbukira mikate isanu ija ya anthu aja zikwi zisanu, ndi madengu angati munawatola?


Koma anati kwa iwo, Muwapatse chakudya ndinu. Koma anati, Ife tilibe mikate, koma isanu yokha, ndi nsomba ziwiri zokha; kapena timuke ife kukagulira anthu awa onse zakudya.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa