Mateyu 14:16 - Buku Lopatulika16 Koma Yesu anati kwa iwo, Iwo alibe chifukwa cha kumukira, apatseni ndinu adye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Koma Yesu anati kwa iwo, Iwo alibe chifukwa cha kumukira, apatseni ndinu adye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Koma Yesu adaŵauza kuti, “Palibe chifukwa choti achokere. Inuyo apatseni chakudya.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Yesu anawayankha kuti, “Sikofunika kuti azipita. Inuyo muwapatse kanthu kuti adye.” Onani mutuwo |