Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 14:16 - Buku Lopatulika

16 Koma Yesu anati kwa iwo, Iwo alibe chifukwa cha kumukira, apatseni ndinu adye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Koma Yesu anati kwa iwo, Iwo alibe chifukwa cha kumukira, apatseni ndinu adye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Koma Yesu adaŵauza kuti, “Palibe chifukwa choti achokere. Inuyo apatseni chakudya.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Yesu anawayankha kuti, “Sikofunika kuti azipita. Inuyo muwapatse kanthu kuti adye.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 14:16
10 Mawu Ofanana  

Alipo wogawira, nangolemerabe; aliponso womana chomwe ayenera kupatsa nangosauka.


Gawira asanu ndi awiri ngakhale asanu ndi atatu; pakuti sudziwa choipa chanji chidzaoneka pansi pano.


Ndipo pamene panali madzulo, ophunzira ake anafika kwa Iye, nanena, Malo ano nga chipululu, ndipo nthawi yapita tsopano; kauzeni makamuwo amuke, apite kumidzi kukadzigulira okha kamba.


Koma iwo ananena kwa Iye, Ife tilibe kanthu pano koma mikate isanu, ndi nsomba ziwiri.


Koma iye anayankha nanena kwa iwo, Iye amene ali nao malaya awiri apatse kwa iye amene alibe; ndi iye amene ali nazo zakudya achite chomwecho.


Pakuti popeza Yudasi anali nalo thumba, ena analikuyesa kuti Yesu ananena kwa iye, Gula zimene zitisowa pachikondwerero; kapena, kuti apatse kanthu kwa aumphawi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa