Mateyu 14:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo Iye anatuluka, naona khamu lalikulu la anthu, nachitira iwo chifundo, nachiritsa akudwala ao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo Iye anatuluka, naona khamu lalikulu la anthu, nachitira iwo chifundo, nachiritsa akudwala ao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Yesu adatuluka m'chombomo, ndipo pamene adaŵaona anthu ambirimbiriwo, adaŵamvera chifundo, nayamba kuchiritsa amene ankadwala. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Yesu atafika ku mtunda, ndi kuona gulu lalikulu la anthu, Iye anamva nawo chifundo ndipo anachiritsa odwala awo. Onani mutuwo |