Mateyu 14:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo anautenga mutu wake m'mbalemo, naupatsa buthulo: ndipo iye anamuka nao kwa amake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo anautenga mutu wake m'mbalemo, naupatsa buthulo: ndipo iye anamuka nao kwa amake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Mutuwo adautengera m'mbale nakaupereka kwa mtsikana uja, mtsikanayo nkukaupereka kwa mai wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Mutu wake anawubweretsa mʼmbale ndi kumupatsa mtsikanayo amene anawutengera kwa amayi ake. Onani mutuwo |