Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 14:10 - Buku Lopatulika

10 ndipo anatumiza mnyamata, namdula mutu Yohane m'nyumba yandende.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 ndipo anatumiza mnyamata, namdula mutu Yohane m'nyumba yandende.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Tsono adatuma munthu kuti akamdule mutu Yohaneyo m'ndende.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 ndipo anakadula mutu wa Yohane mʼndende.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 14:10
12 Mawu Ofanana  

koma ananyodola mithenga ya Mulungu, napeputsa mau ake, naseka aneneri ake, mpaka ukali wa Yehova unaukira anthu ake, mpaka panalibe cholanditsa.


Ndapanda ana anu mwachabe; sanamvere kulanga; lupanga lanu ladya aneneri anu, monga mkango wakuononga.


Ndipo anautenga mutu wake m'mbalemo, naupatsa buthulo: ndipo iye anamuka nao kwa amake.


Ndipo mfumuyo anagwidwa ndi chisoni; koma chifukwa cha malumbiro ake, ndi cha iwo anali naye pachakudya, analamulira upatsidwe;


koma ndinena kwa inu, kuti Eliya anadza kale, ndipo iwo sanamdziwe iye, koma anamchitira zonse zimene anazifuna iwo. Ndipo chonchonso Mwana wa Munthu adzazunzidwa ndi iwo.


Koma ndinena ndi inu kuti anafikadi Eliya, ndipo anamchitiranso zilizonse iwo anazifuna, monga kwalembedwa za iye.


Ndipo Herode anati, Yohane ndinamdula mutu ine; koma uyu ndani ndikumva zotere za iye? Ndipo anafunafuna kumuona Iye.


Ndipo pamene zidatsiriza umboni wao chilombo chokwera kutuluka m'chiphompho chakuya chidzachita nazo nkhondo, ndipo chidzazigonjetsa, ndi kupha izo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa