Mateyu 14:10 - Buku Lopatulika10 ndipo anatumiza mnyamata, namdula mutu Yohane m'nyumba yandende. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 ndipo anatumiza mnyamata, namdula mutu Yohane m'nyumba yandende. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Tsono adatuma munthu kuti akamdule mutu Yohaneyo m'ndende. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 ndipo anakadula mutu wa Yohane mʼndende. Onani mutuwo |