Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 13:56 - Buku Lopatulika

56 Ndipo alongo ake sali ndife onsewa? Ndipo Iyeyo adazitenga zinthu zonsezi kuti?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

56 Ndipo alongo ake sali ndife onsewa? Ndipo Iyeyo adazitenga zinthu zonsezi kuti?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

56 Kodi suja alongo ake onse ali nafe pompano? Nanga tsono zonsezi adazitenga kuti?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

56 Kodi alongo ake onse sali ndi ife? Tsono ndi kuti kumene anazitenga zinthu izi?”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 13:56
2 Mawu Ofanana  

Ndipo iwo anakhumudwa chifukwa cha Iye. Koma Yesu anati kwa iwo, Mneneri sakhala wopanda ulemu koma kudziko la kwao ndiko, ndi kubanja kwake.


Si mmisiri wa mitengo uyu, mwana wa Maria, mbale wao wa Yakobo, ndi Yose, ndi Yudasi, ndi Simoni? Ndipo alongo ake sali nafe pano kodi? Ndipo anakhumudwa ndi Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa