Mateyu 13:49 - Buku Lopatulika49 Padzatero pa chimaliziro cha nthawi ya pansi pano: angelo adzatuluka, nadzawasankhula oipa pakati pa abwino, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 Padzatero pa chimaliziro cha nthawi ya pansi pano: angelo adzatuluka, nadzawasankhula oipa pakati pa abwino, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 Zidzateronso pa kutha kwa dziko lino lapansi. Angelo adzabwera nadzachotsa anthu ochimwa pakati pa anthu olungama, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 Umu ndi mmene kudzakhalira pakutha kwa dziko. Angelo adzabwera ndi kulekanitsa oyipa ndi olungama. Onani mutuwo |