Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 13:50 - Buku Lopatulika

50 nadzawataya m'ng'anjo yamoto; komweko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

50 nadzawataya m'ng'anjo yamoto; komweko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

50 nkumaŵaponya m'ng'anjo ya moto. Kumeneko adzalira ndi kukukuta mano.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

50 Ndipo oyipa adzawaponya mʼngʼanjo ya moto kumene kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 13:50
8 Mawu Ofanana  

ndipo aliyense wosagwadira ndi kulambira, adzaponyedwa nthawi yomweyo m'kati mwa ng'anjo yotentha yamoto.


ndipo adzawataya iwo m'ng'anjo yamoto; kumeneko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.


Mwamvetsa zonsezi kodi? Iwo anati kwa Iye, Inde.


koma anawo a Ufumu adzatayidwa kumdima wakunja; komweko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa