Mateyu 13:47 - Buku Lopatulika47 Ndiponso, Ufumu wa Kumwamba uli wofanana ndi khoka loponyedwa m'nyanja, ndi kusonkhanitsa pamodzi za mitundu yonse; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201447 Ndiponso, Ufumu wa Kumwamba uli wofanana ndi khoka loponyedwa m'nyanja, ndi kusonkhanitsa pamodzi za mitundu yonse; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa47 “Ufumu wakumwamba ulinso ngati khoka limene anthu amaliponya m'nyanja, ndipo limagwira nsomba za mitundu yonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero47 “Komanso Ufumu wakumwamba ufanana ndi khoka limene linaponyedwa mʼnyanja ndipo linakola mitundu yonse ya nsomba. Onani mutuwo |