Mateyu 13:45 - Buku Lopatulika45 Ndiponso Ufumu wa Kumwamba uli wofanana ndi munthu wa malonda, wakufuna ngale zabwino: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Ndiponso Ufumu wa Kumwamba uli wofanana ndi munthu wa malonda, wakufuna ngale zabwino: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 “Ndiponso Ufumu wakumwamba uli ngati munthu wamalonda wonka nafunafuna ngale zokongola zamtengowapatali. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 “Komanso Ufumu wakumwamba ufanana ndi wogulitsa malonda amene amafuna ngale zabwino. Onani mutuwo |