Mateyu 13:43 - Buku Lopatulika43 Pomwepo olungamawo adzawalitsa monga dzuwa, mu Ufumu wa Atate wao. Amene ali ndi makutu amve. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201443 Pomwepo olungamawo adzawalitsa monga dzuwa, mu Ufumu wa Atate wao. Amene ali ndi makutu amve. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa43 Tsono anthu olungama adzaŵala ngati dzuŵa mu Ufumu wa Atate ao. Amene ali ndi makutu, amve! Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero43 Pamenepo olungama adzawala ngati dzuwa mu ufumu wa Atate awo. Amene ali ndi makutu amve.” Onani mutuwo |