Mateyu 13:42 - Buku Lopatulika42 ndipo adzawataya iwo m'ng'anjo yamoto; kumeneko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201442 ndipo adzawataya iwo m'ng'anjo yamoto; kumeneko kudzakhala kulira ndi kukukuta mano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa42 nadzaŵaponya m'ng'anjo ya moto. Kumeneko adzalira ndi kukukuta mano. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero42 Adzawaponya mʼngʼanjo yamoto kumene kudzakhala kulira ndi kukuta mano. Onani mutuwo |