Mateyu 13:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo m'kufesa kwake zina zinagwa m'mbali mwa njira, ndipo zinadza mbalame, nkulusira izo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo m'kufesa kwake zina zinagwa m'mbali mwa njira, ndipo zinadza mbalame, nizilusira izo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Akufesa choncho, mbeu zina zidagwera m'njira, ndipo mbalame zidabwera nkuzitolatola. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Akufesa, zina zinagwera mʼmbali mwa njira ndipo mbalame zinabwera ndi kuzidya. Onani mutuwo |