Mateyu 13:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo Iye anawauzira zinthu zambiri m'mafanizo, nanena, Onani, wofesa anatuluka kukafesa mbeu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo Iye anawauzira zinthu zambiri m'mafanizo, nanena, Onani, wofesa anatuluka kukafesa mbeu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Yesu adalankhula nawo zambiri m'mafanizo. Adati, “Munthu wina adaapita kukafesa mbeu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamenepo Iye anawawuza zinthu zambiri mʼmafanizo ndi kuti, “Mlimi anapita kukafesa mbewu zake. Onani mutuwo |