Mateyu 13:37 - Buku Lopatulika37 Ndipo Iye anayankha nati, Wofesa mbeu yabwino ndiye Mwana wa Munthu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201437 Ndipo Iye anayankha nati, Wofesa mbeu yabwino ndiye Mwana wa Munthu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa37 Yesu adati, “Wofesa mbeu zabwino uja ndi Mwana wa Munthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero37 Iye anayankha nati, “Munthu amene anafesa mbewu yabwino ndi Mwana wa Munthu. Onani mutuwo |