Mateyu 13:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo munda ndiwo dziko lapansi; ndi mbeu yabwino ndiyo ana a Ufumuwo; ndi namsongole ndiye ana a woipayo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo munda ndiwo dziko lapansi; ndi mbeu yabwino ndiyo ana a Ufumuwo; ndi namsongole ndiye ana a woipayo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Munda uja ndi dziko lino lapansi. Mbeu zabwino zija ndi anthu ake a Ufumu wakumwamba. Namsongole uja ndi anthu ake a Woipa uja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Munda ndi dziko lapansi ndipo mbewu yabwino ndi ana a ufumu. Namsongole ndi ana a woyipayo. Onani mutuwo |