Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 13:26 - Buku Lopatulika

26 Koma pamene mmera unakula, nubala chipatso, pomwepo anaonekeranso namsongole.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Koma pamene mmera unakula, nubala chipatso, pomwepo anaonekeranso namsongole.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Tsono pamene mmera udakula nkuyamba kuchita njere, namsongole uja nayenso adayamba kuwoneka.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Pamene tirigu anamera ndi kutulutsa ngala, namsongole anaonekanso.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 13:26
4 Mawu Ofanana  

Ndipo inaphuka, nikhala mpesa wotambalala waufupi msinkhu, nthambi zake zinapindikira momwe, ndi mizu yake pansi pake, nikhala mpesa, nuonetsa nthambi ndi kuphuka mphukira.


koma m'mene anthu analinkugona, mdani wake anadza, nafesa namsongole pakati pa tirigu, nachokapo.


Ndipo anyamata ake a mwini nyumbayo anadza, nati kwa iye, Mbuye, kodi simunafese mbeu zabwino m'munda mwanu? Nanga wachokera kuti namsongoleyo?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa