Mateyu 13:26 - Buku Lopatulika26 Koma pamene mmera unakula, nubala chipatso, pomwepo anaonekeranso namsongole. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Koma pamene mmera unakula, nubala chipatso, pomwepo anaonekeranso namsongole. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Tsono pamene mmera udakula nkuyamba kuchita njere, namsongole uja nayenso adayamba kuwoneka. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Pamene tirigu anamera ndi kutulutsa ngala, namsongole anaonekanso. Onani mutuwo |