Mateyu 13:25 - Buku Lopatulika25 koma m'mene anthu analinkugona, mdani wake anadza, nafesa namsongole pakati pa tirigu, nachokapo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 koma m'mene anthu analinkugona, mdani wake anadza, nafesa namsongole pakati pa tirigu, nachokapo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Koma anthu onse ali m'tulo, mdani wake adabwera, nkufesa namsongole pakati pa tirigu, nachokapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Koma aliyense akugona usiku mdani wake anabwera ndi kufesa namsongole pakati pa tirigu ndipo anachoka. Onani mutuwo |