Mateyu 12:6 - Buku Lopatulika6 Koma ndinena kwa inu, kuti wakuposa Kachisiyo ali pompano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Koma ndinena kwa inu, kuti wakuposa Kachisiyo ali pompano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ndipotu ndikunenetsa kuti pali wina pano woposa Nyumba ya Mulunguyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Ine ndikuwuzani kuti wamkulu kuposa Nyumba ya Mulunguyo ali pano. Onani mutuwo |