Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 12:48 - Buku Lopatulika

48 Koma Iye anayankha, nati kwa iye wonenayo, Amai wanga ndani, ndipo abale anga ndi ayani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

48 Koma Iye anayankha, nati kwa iye wonenayo, Amai wanga ndani, ndipo abale anga ndi ayani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

48 Yesu adamuyankha kuti, “Kodi ine amai anga ndani? Ndipo abale anga ndani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

48 Iye anayankha kuti, “Amayi anga ndani ndipo abale anga ndi ndani?”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 12:48
9 Mawu Ofanana  

Iye wakukonda atate wake, kapena amake koposa Ine, sayenera Ine, ndipo iye wakukonda mwana wake wamwamuna, kapena wamkazi koposa Ine, sayenera Ine.


Ndipo munthu anati kwa Iye, Onani, amai wanu ndi abale anu aima pabwalo, nafuna kulankhula nanu.


Ndipo anatambalitsa dzanja lake pa ophunzira ake, nati, Penyani amai wanga ndi abale anga!


Ndipo Iye anati kwa iwo, Kuli bwanji kuti munalikundifunafuna Ine? Simunadziwa kodi kuti kundiyenera Ine ndikhale m'zake za Atate wanga?


Ndipo Yesu anakulabe m'nzeru ndi mumsinkhu, ndi m'chisomo cha pa Mulungu ndi cha pa anthu.


Kotero kuti ife sitidziwanso munthu tsopano monga mwa thupi; ndipo ngati tazindikira Khristu monga mwa thupi, koma tsopano sitimzindikiranso motero.


amene anati za atate wake ndi amai wake, sindinamuone; Sanazindikire abale ake, sanadziwe ana ake omwe; popeza anasamalira mau anu, nasunga chipangano chanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa