Mateyu 12:48 - Buku Lopatulika48 Koma Iye anayankha, nati kwa iye wonenayo, Amai wanga ndani, ndipo abale anga ndi ayani? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201448 Koma Iye anayankha, nati kwa iye wonenayo, Amai wanga ndani, ndipo abale anga ndi ayani? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa48 Yesu adamuyankha kuti, “Kodi ine amai anga ndani? Ndipo abale anga ndani?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero48 Iye anayankha kuti, “Amayi anga ndani ndipo abale anga ndi ndani?” Onani mutuwo |