Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 12:47 - Buku Lopatulika

47 Ndipo munthu anati kwa Iye, Onani, amai wanu ndi abale anu aima pabwalo, nafuna kulankhula nanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

47 Ndipo munthu anati kwa Iye, Onani, amai wanu ndi abale anu aima pabwalo, nafuna kulankhula nanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

47 Tsono munthu wina adauza Yesu kuti, “Amai anu ndi abale anu ali panjapa, akufuna kulankhula nanu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

47 Wina anamuwuza Iye kuti, “Amayi ndi abale anu ayima kunjaku akufuna kuyankhulana nanu.”

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 12:47
2 Mawu Ofanana  

Pamene Iye anali chilankhulire ndi makamu, onani, amake ndi abale ake anaima panja, nafuna kulankhula naye.


Koma Iye anayankha, nati kwa iye wonenayo, Amai wanga ndani, ndipo abale anga ndi ayani?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa