Mateyu 11:9 - Buku Lopatulika9 Koma munatulukiranji? Kukaona mneneri kodi? Indetu, ndinena kwa inu, wakuposa mneneri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma munatulukiranji? Kukaona mneneri kodi? Indetu, ndinena kwa inu, wakuposa mneneri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Tanenanitu, mudaati mukaona chiyani? Mneneri kodi? Zoonadi, ndipo ndikunenetsa kuti mudakaona woposa mneneri amene. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Nanga munkapita kukaona chiyani? Mneneri kodi? Inde ndikuwuzani kuti munkakaona woposa mneneri. Onani mutuwo |