Mateyu 11:3 - Buku Lopatulika3 nati kwa Iye, Inu ndinu wakudza kodi, kapena tiyembekezere wina? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 nati kwa Iye, Inu ndinu wakudza kodi, kapena tiyembekezere wina? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 “Kodi Inu ndinu uja ankati adzabwerayu, kapena tiziyembekezera wina?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Anamufunsa kuti, “Kodi Inu ndinu uja ankanena kuti mudzabwerayu kapena tidikire wina?” Onani mutuwo |