Mateyu 11:2 - Buku Lopatulika2 Koma Yohane, pakumva m'nyumba yandende ntchito za Khristu, anatumiza ophunzira ake mau, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Koma Yohane, pakumva m'nyumba yandende ntchito za Khristu, anatumiza ophunzira ake mau, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Pamene Yohane Mbatizi anali m'ndende, adaamva zimene Khristu uja ankachita. Choncho adatuma ophunzira ake ena kwa Iye kukamufunsa kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Yohane ali mʼndende anamva zimene Khristu ankachita, ndipo anatumiza ophunzira ake kukamufunsa Iye. Onani mutuwo |