Mateyu 11:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo Yesu anayankha, nanena nao, Mukani mubwezere mau kwa Yohane zimene muzimva ndi kuziona: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo Yesu anayankha, nanena nao, Mukani mubwezere mau kwa Yohane zimene muzimva ndi kuziona: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Yesu adati, “Pitani, kamuuzeni Yohane zimene mukuzimva ndi kuziwona. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Yesu anayankha kuti, “Bwererani ndi kukamuwuza Yohane zimene mwamva ndi kuona. Onani mutuwo |