Mateyu 11:24 - Buku Lopatulika24 Komanso ndinena kwa inu kuti tsiku la kuweruza, mlandu wake wa Sodomu udzachepa ndi wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Komanso ndinena kwa inu kuti tsiku la kuweruza, mlandu wake wa Sodomu udzachepa ndi wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Koma ndikunenetsa kuti pa tsiku la chiweruzo Mulungu adzachitako chifundo polanga Sodomu koposa polanga iwe.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Koma Ine ndikuwuzani kuti pa tsiku la chiweruziro mlandu wa Sodomu udzachepako kusiyana ndi wanu.” Onani mutuwo |