Mateyu 11:22 - Buku Lopatulika22 Komanso ndinena kwa inu kuti tsiku la kuweruza mlandu wao wa Tiro ndi Sidoni udzachepa ndi wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Komanso ndinena kwa inu kuti tsiku la kuweruza mlandu wao wa Tiro ndi Sidoni udzachepa ndi wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Koma ndikunenetsa kuti pa tsiku lachiweruzo, Mulungu adzachitako chifundo polanga Tiro ndi Sidoni, koposa polanga inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Koma ndikuwuzani inu kuti pa tsiku lachiweruzo mlandu wa Turo ndi Sidoni udzachepako kusiyana ndi wanu. Onani mutuwo |