Mateyu 11:17 - Buku Lopatulika17 Ndi kuti, Tinakulizirani inu zitoliro, ndipo inu simunavine; tinabuma maliro, ndipo inu simunalire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndi kuti, Tinakulizirani inu zitoliro, ndipo inu simunavina; tinabuma maliro, ndipo inu simunalira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 “ ‘Tidaakuimbirani ng'oma yaukwati, bwanji inu osavina? Tidaabuma maliro, bwanji inu osalira?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 “ ‘Tinakuyimbirani zitoliro, koma inu simunavine; ife tinayimba nyimbo zamaliro, koma inu simunalire.’ Onani mutuwo |