Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 10:9 - Buku Lopatulika

9 Musadzitengere ndalama zagolide, kapena zasiliva, kapena zakobiri m'malamba mwanu;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Musadzitengere ndalama zagolide, kapena zasiliva, kapena zakobiri m'malamba mwanu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Musatenge ndalama m'zikwama, kaya nzagolide, kaya nzasiliva, kaya nzakopala.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 “Musatenge ndalama zagolide kapena zasiliva kapena zakopala mʼzikwama mwanu;

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 10:9
7 Mawu Ofanana  

Chiritsani akudwala, ukitsani akufa, konzani akhate, tulutsani ziwanda: munalandira kwaulere, patsani kwaulere.


Ndipo anadziitanira khumi ndi awiriwo, nayamba kuwatumiza iwo awiriawiri; nawapatsa mphamvu pa mizimu yonyansa;


Ndipo anati kwa iwo, Pamene ndinakutumizani opanda thumba la ndalama, ndi thumba la kamba, ndi nsapato, munasowa kanthu kodi? Anati iwo, Iai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa