Mateyu 10:8 - Buku Lopatulika8 Chiritsani akudwala, ukitsani akufa, konzani akhate, tulutsani ziwanda: munalandira kwaulere, patsani kwaulere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Chiritsani akudwala, ukitsani akufa, konzani akhate, tulutsani ziwanda: munalandira kwaulere, patsani kwaulere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Muzikachiritsa odwala, muzikaukitsa akufa, muzikachotsa khate, muzikatulutsa mizimu yoipa. Mwalandira mwaulere, kaperekeni mwaulere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Chiritsani odwala, ukitsani akufa, chiritsani akhate, tulutsani ziwanda. Munalandira kwaulere, perekani kwaulere. Onani mutuwo |