Mateyu 10:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo pamene mulikupita lalikani kuti, Ufumu wa Kumwamba wayandikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo pamene mulikupita lalikani kuti, Ufumu wa Kumwamba wayandikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pitani, muzikalalika kuti, ‘Mulungu ali pafupi kukhazikitsa ufumu wake tsopano.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pamene mukupita, muzikalalikira uthenga uwu: ‘Ufumu wakumwamba wayandikira.’ Onani mutuwo |