Mateyu 10:10 - Buku Lopatulika10 kapena thumba la kamba la kunjira, kapena malaya awiri, kapena nsapato, kapena ndodo; pakuti wantchito ayenera kulandira zakudya zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 kapena thumba la kamba la kunjira, kapena malaya awiri, kapena nsapato, kapena ndodo; pakuti wantchito ayenera kulandira zakudya zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Musatenge thumba lapaulendo, kapena mikanjo iŵiri, kapena nsapato, kapena ndodo. Paja wantchito ngwoyenera kulandira zosoŵa zake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 musatenge thumba la paulendo, kapena malaya awiri kapena nsapato kapena ndodo; pakuti wantchito ayenera kulandira chakudya chake. Onani mutuwo |