Mateyu 10:33 - Buku Lopatulika33 Koma yense amene adzandikana Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzamkana iye pamaso pa Atate wanga wa Kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Koma yense amene adzandikana Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzamkana iye pamaso pa Atate wanga wa Kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Koma aliyense wondikana pamaso pa anthu kuti Ine sandidziŵa, Inenso ndidzamkana pamaso pa Atate anga amene ali Kumwamba kuti sindimdziŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Koma iye amene andikana Ine pamaso pa anthu, Inenso ndidzamukana pamaso pa Atate anga akumwamba. Onani mutuwo |