Mateyu 10:31 - Buku Lopatulika31 Chifukwa chake musamaopa; inu mupambana mpheta zambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Chifukwa chake musamaopa; inu mupambana mpheta zambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Choncho musati muziwopa ai. Ndinu a mtengo woposa atimba ambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Potero musaope; inu ndinu a mtengo woposa mbalame zambiri. Onani mutuwo |