Mateyu 10:30 - Buku Lopatulika30 komatu inu, matsitsi onse a m'mutu mwanu awerengedwa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 komatu inu, matsitsi onse a m'mutu mwanu awerengedwa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Inuyotu ngakhale tsitsi lomwe la kumutu kwanu adaliŵerenga lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Ndipo ngakhale tsitsi la mʼmutu mwanu linawerengedwa kale. Onani mutuwo |