Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 10:29 - Buku Lopatulika

29 Kodi mpheta ziwiri sizigulidwa kakobiri? Ndipo imodzi ya izo siigwa pansi popanda Atate wanu:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 Kodi mpheta ziwiri sizigulidwa kakobiri? Ndipo imodzi ya izo siigwa pansi popanda Atate wanu:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 Suja amagulitsa atimba aŵiri kandalama kamodzi? Komabe palibe ndi m'modzi yemwe amene angagwe pansi, Atate anu osadziŵa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Kodi suja amagulitsa mbalame ziwiri ndi ndalama imodzi? Koma palibe imodzi ya izo imene idzagwa pansi wopanda chifuniro cha Atate anu.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 10:29
5 Mawu Ofanana  

Indetu ndinena ndi iwe, sudzatulukamo konse, koma utalipa kakobiri kakumaliza ndiko.


Yang'anirani mbalame za kumwamba, kuti sizimafesa ai, kapena sizimatema ai, kapena sizimatutira m'nkhokwe; ndipo Atate wanu wa Kumwamba azidyetsa. Nanga inu mulibe kusiyana nazo kuziposa kodi?


Ndipo anadza mkazi wamasiye waumphawi, ndipo iye anaponyamo tindalama tiwiri tating'ono tokwanira kakobiri kamodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa