Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 1:4 - Buku Lopatulika

4 ndi Ramu anabala Aminadabu; ndi Aminadabu anabala Nasoni; ndi Nasoni anabala Salimoni;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 ndi Ramu anabala Aminadabu; ndi Aminadabu anabala Nasoni; ndi Nasoni anabala Salimoni;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Ramu adabereka Aminadabu, Aminadabu adabereka Nasoni, Nasoni adabereka Salimoni.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Aramu anabereka Aminadabu, Aminadabu anabereka Naasoni, Naasoni anabereka Salimoni.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 1:4
10 Mawu Ofanana  

Wa Yuda, Nasoni mwana wa Aminadabu.


Ndipo anayamba kuyenda ambendera ya chigono cha ana a Yuda monga mwa magulu ao; woyang'anira gulu lake ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.


Ndipo iwo akumanga mahema ao ku m'mawa kotuluka dzuwa ndiwo a mbendera ya chigono cha Yuda, monga mwa makamu ao; ndipo kalonga wa ana Yuda ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.


Wakubwera nacho chopereka chake tsiku loyamba ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu, wa fuko la Yuda:


ndi nsembe yoyamika, ng'ombe ziwiri, nkhosa zamphongo zisanu, atonde asanu, anaankhosa asanu a chaka chimodzi; ndicho chopereka cha Nasoni mwana wa Aminadabu.


ndi Yuda anabala Perezi ndi Zera mwa Tamara; ndi Perezi anabala Hezironi; ndi Hezironi anabala Ramu;


ndi Salimoni anabala Bowazi mwa Rahabu; ndi Bowazi anabala Obede mwa Rute; ndi Obede anabala Yese;


mwana wa Yese, mwana wa Obede, mwana wa Bowazi, mwana wa Salimoni, mwana wa Nasoni,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa